Malawi Congress Party
  • Home
  • About us
  • News
  • Media
  • Events
  • Contact us
Get involved
Police houses, Mangochi

Police houses, Mangochi

October 5, 2021 0 Comments by admin in Uncategorized

Tawonani kukongola kwa nyumba zanyuwani za apolisi uko ku Malemia Camp ku Malindi, boma la Mangochi. Ndithutu apolisi athu nawo adzikhala munyumba zolemekezeka, zokongola komanso za zipangizo zamakono mkati.Kwantere ndithu Dr. Lazarus Chakwera akuwonetsetsa kuti miyoyo ya apolisi, asilikali ndi onse ogwira ntchito zachitetezo mudziko lino isinthe. Pa ground pakuwala!

Read More