Enukwenu Bridge in Mzimba District
The Minister of Transport and Public Works Hon Jacob Hara today on 1st March inspected Enukwenu Bridge in Mzimba District. Enukwenu Bridge is the river that connects Mzimba North to Rumphi, Karonga ,Chitupa even to our neighboring country Tanzania.#BuildANewMalawi

Area 32, Lilongwe
There will be hotels, recreation facilities, a shopping mall, apartments, office buildings, and a modern multi-story carpark….
Read MoreMozambique-Malawi Power Interconnection
Their Excellencies Filipe Jacinto Nyusi, President of The Republic of Mozambique, And Dr. Lazarus McCarthy Chakwera, President of the Republic of Malawi, were this morning at Phombeya in Balaka District to launch the Mozambique-Malawi Power Interconnection Project. The project will involve the construction of a 218-kilometre 400kV High Voltage Alternating Current transmission line from Matambo in Tete Province in Central Mozambique, past the Malawian border in Mwanza and all the way to Phombeya, Balaka, from which it will connect to other parts of the country.
Read MoreSolar Power Station, Salima.
Magetsi ayatsidwa lero! President wathu anawonetstetsa kuti ntchito yomwe inabweletsedwa mu dziko lino ndi President Joyce Banda komanso kuyambidwa pansi pa President Peter Mutharika imalizidwe mwa makono ndiponso mosasolora olo one Tambala. Ndithu kuyambira chaka chino, national grid yathu yawonjezedwa ndi 60 Megawatts ndipo zoti magetsi amathima mwachisawawa zikhala mbiri yakale.Kumanyadira dziko lanu, aMalawi. Zotelezitu mulibe mmayiko ambiri ndipo power station imeneyi ndi imodzi mwa zazikulu kwambiri mu Africa ndipo si yokhayitu kwathu kuno; nakonso ku Golomoti uko ilipo yina. Kwanteretu chidzuwa chathuchi tachipezera ntchito ndipo tonse tipindura pogwilitsa magetsi osawononga chilengedwe. Pa ground padziwala ngati masana koma uli usiku!
Read MoreConstruction of Port, Likoma Island.
Ports are catalysts for economic development because they enable trade, facilitate the movement of people, goods and services and support supply chains. Dr. Chakwera promised the people of Likoma Island that his administration would build a port on the island. The new port is currently under construction and the island will soon wear a new face. Kwantere basi ulendo wopita ndikuchokera ku Likoma waphwekeratu! Pa chilumba napo pakuwala! Please share this post with your friends and families.
Read MorePolice houses, Mangochi
Tawonani kukongola kwa nyumba zanyuwani za apolisi uko ku Malemia Camp ku Malindi, boma la Mangochi. Ndithutu apolisi athu nawo adzikhala munyumba zolemekezeka, zokongola komanso za zipangizo zamakono mkati.Kwantere ndithu Dr. Lazarus Chakwera akuwonetsetsa kuti miyoyo ya apolisi, asilikali ndi onse ogwira ntchito zachitetezo mudziko lino isinthe. Pa ground pakuwala!
Read More